Friday, May 9, 2025
spot_imgspot_img

Top 5 This Week

spot_img

Related Posts

Mutharika asankha wankulu wa bungwe lazachisankho la MEC

President Peter Mutharika wasankha Justice Jane Ansah kukhala wapampando wa bungwe lazachisankho la Malawi Electoral Commission (MEC).

Ansah walowa m’malo mwa malemu Maxon Mbendera omwe anamwalira mwezi watha atangogwa pa mpando ku Lilongwe akugwila nchito zina zokhuza ofesi yake.

Mlembi wamkulu wa boma a George Mkondiwa ati kusankhudwaku kukuyambila lero.

Justice Ansah anali judge ku bwalo la apilo.

LEAVE A REPLY

Please enter your comment!
Please enter your name here

Popular Articles